Malawi Muslims Official Website
No Result
View All Result
  • Login
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World
Contact Us
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World
No Result
View All Result
Malawi Muslims Official Website
No Result
View All Result
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World
Home Featured
Sheikh Idrissa Muhammad Apempha Asilamu Kuti Ayambe Kuthandiza Bungwe la MAM

Sheikh Idrissa Muhammad Apempha Asilamu Kuti Ayambe Kuthandiza Bungwe la MAM

Marshall Dyton by Marshall Dyton
4 years ago
in Featured, Religion
Reading Time: 2 mins read
A A
0
0
SHARES
0
VIEWS
Share on FacebookShare on TwitterShare on Whatsapp

Wapampando wa bungwe la Muslim Association of Malawi (MAM) Sheikh Idrissa Muhammad wapempha asilamu onse mdziko muno kuti ayambe kuthandiza bungweli.

RELATED POSTS

Are We Too Small for Political Courage?

๐—›๐—œ๐—ฆ๐—ง๐—ข๐—ฅ๐—œ๐—– ๐—ฉ๐—œ๐—–๐—ง๐—ข๐—ฅ๐—ฌ: ๐—–๐—ต๐—ฎ๐—ธ๐˜„๐—ฒ๐—ฟ๐—ฎ ๐——๐—ฒ๐—น๐—ถ๐˜ƒ๐—ฒ๐—ฟ๐˜€ ๐—ช๐—ต๐—ฎ๐˜ ๐Ÿฒ๐Ÿฌ ๐—ฌ๐—ฒ๐—ฎ๐—ฟ๐˜€ ๐—ผ๐—ณ ๐—Ÿ๐—ฒ๐—ฎ๐—ฑ๐—ฒ๐—ฟ๐˜€ ๐—ก๐—ฒ๐˜ƒ๐—ฒ๐—ฟ ๐—–๐—ผ๐˜‚๐—น๐—ฑโ€”๐—ข๐—ณ๐—ณ๐—ถ๐—ฐ๐—ถ๐—ฎ๐—น ๐—ฅ๐—ฒ๐—ฐ๐—ผ๐—ด๐—ป๐—ถ๐˜๐—ถ๐—ผ๐—ป ๐—ผ๐—ณ ๐—˜๐—ถ๐—ฑ ๐—ฎ๐—น-๐—”๐—ฑ๐—ต๐—ฎ

The Wrong Sacrifice: How Muslims in Malawi Are Slaughtering Community Unity Instead of Goats This Eid

Sheikh Muhammad amalankhula izi pamsonkhano wa atolankhani womwe anachititsa lero mumzinda wa Blantyre.

Mtsogoleri wa asilamuyu wati ndizomvetsa chisoni kuti pali kagulu kena ka asilamu komwe kakumangonena zoyipa za MAM, kunena kuti akuluakulu abungweli akusakaza ndalama chikhalirenicho sanasonkheko ndalama iliyonse.

Iwo anati poyerekeza ndi mabungwe ena oti si asilamu, MAM imadalira thandizo lake kuchokera kwa mabungwe akunja kwa dziko lino ndipo ndalama zake zimakhala ndi ntchito zake kale.

“Asilamu tisinthe maganizidwe athu. Tisamangokamba zoipa za bungwe, kulikakamiza kuti lipange zinthu zoti silingakwanitse kumakhala kuti palibe chomwe timapereka ku bungweli. Kodi ndi ndani ananena kuti poti ndife asilamu ndiye tizingolandira za ulere koma kupereka ayi popeza kuti Chipembedzo chachisilamu ndiye chimalimbikitsa kuperekako? Tangoganizani nthawi ya Qurban munthu kumachoka kutali ngati ku Lilongwe, kuthira mafuta muchigalimoto chodhula kubwera ku Blantyre kukalandira Mbuzi imodzi? Ndalama mwagula mafuta sangakwanitse kugula Mbuzi olo imodzi zoona? Izi sizoona ayi,” atero mtsogoleriyu.

Sheikh Muhammad anawonjezerapo kunena kuti pamene amatenga mpandowu zaka khumi zapitazo analamula atsogoleri amadera onse mdziko muno kuti atsegule ma akaunti akubanki ndi cholinga choti asilamu ayambe kusonkha ndipo kuti ndalamayo izigwiritsidwa popangira zitukuko zing’onozing’ono za deralo.

“Kutha kumva chisoni kumva kuti chitsegulireni akauntiyi sikunaloweko olo ndalama iliyonse mpaka abanki anatseka ma akaunti. Koma lero akubwera ndikumandinyoza ine kuti ndikuba ndalama za asilamu mdziko muno. Ndalama zake ziti popeza simunaperekeko ndalama iliyonse?” Anafunsa motero Sheikh Muhammad.

ADVERTISEMENT

Mtsogoleriyu anapitilizanso kunena kuti kwa amene ali ndi umboni okwanira woti iwo akusakaza ndalama za asilamu apite ndi umboni ku polisi yomwe ali nayo pafupi kukang’amala.

“Akanene kuti Sheikh Idrissa Muhammad analandira ndalama izi za asilamu komwe ntchito yake sanagwiritse ndipo umboni wake ndi uwu mmalo momangolankhulalankhula mmasamba amchezo,” atero mtsogoleri wa asilamuyu.

Iye anati sakuletsa aliyense kupereka madandaulo ake ku bungweli, kunena kuti khomo ndi lotsegula.

“Atha kuyamba kuwapeza atsogoleri amadela akukhala omwe adzatenge nkhawazo kupititsa kulikulu. Sindinganene kuti ndine mNgelo wosalakwa. Ndili ndi zofooka zanga koma tiyeni titsatire njira yoyenera osati kundiopsyeza kuti mundipha. Mundipha chifukwa chani?” Anadandaula motero Sheikh Idrissa Muhammad.

ShareTweetSend

Related Posts

Adil Chilungo
Analysis

Are We Too Small for Political Courage?

by Marshall Dyton
July 24, 2025
0
0

The moment Adil Chilungo walked into that nomination hall on July 24, 2025, he wasn't just carrying his papersโ€”he was...

Read more

๐—›๐—œ๐—ฆ๐—ง๐—ข๐—ฅ๐—œ๐—– ๐—ฉ๐—œ๐—–๐—ง๐—ข๐—ฅ๐—ฌ: ๐—–๐—ต๐—ฎ๐—ธ๐˜„๐—ฒ๐—ฟ๐—ฎ ๐——๐—ฒ๐—น๐—ถ๐˜ƒ๐—ฒ๐—ฟ๐˜€ ๐—ช๐—ต๐—ฎ๐˜ ๐Ÿฒ๐Ÿฌ ๐—ฌ๐—ฒ๐—ฎ๐—ฟ๐˜€ ๐—ผ๐—ณ ๐—Ÿ๐—ฒ๐—ฎ๐—ฑ๐—ฒ๐—ฟ๐˜€ ๐—ก๐—ฒ๐˜ƒ๐—ฒ๐—ฟ ๐—–๐—ผ๐˜‚๐—น๐—ฑโ€”๐—ข๐—ณ๐—ณ๐—ถ๐—ฐ๐—ถ๐—ฎ๐—น ๐—ฅ๐—ฒ๐—ฐ๐—ผ๐—ด๐—ป๐—ถ๐˜๐—ถ๐—ผ๐—ป ๐—ผ๐—ณ ๐—˜๐—ถ๐—ฑ ๐—ฎ๐—น-๐—”๐—ฑ๐—ต๐—ฎ

The Wrong Sacrifice: How Muslims in Malawi Are Slaughtering Community Unity Instead of Goats This Eid

The Stage He Chose: Dr. Namadingo’s Unscripted Performance in Wakata

Finding Balance – How One Nurse’s Story Inspired a Return to Prayer

Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

  • Sheikh Yahya

    Ya Sheikh, Can You Hear Us Weeping? A Community’s Heartfelt Farewell to Sheikh Hubdein Yahya

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Police warn Malawians against sending money to unknown Facebook friends

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Sacred Care: Muslim Nurse’s Mission of Mercy

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • LMJ Medicals for State-of-the-art Hospital

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Trending
  • Comments
  • Latest
Sheikh Yahya

Ya Sheikh, Can You Hear Us Weeping? A Community’s Heartfelt Farewell to Sheikh Hubdein Yahya

April 4, 2025
Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

May 4, 2025
Police warn Malawians against sending money to unknown Facebook friends

Police warn Malawians against sending money to unknown Facebook friends

December 24, 2019
Sacred Care: Muslim Nurse’s Mission of Mercy

Sacred Care: Muslim Nurse’s Mission of Mercy

May 1, 2025

Malawian Muslims Chased at Asian Muslims Miladโ€“un-Nabee Feast

78

Supreme Council of Ulama Says Eid Adha Tuesday

28

Fatima Rajab the Guardian Angel, Abandoned for Refusing to Denounce Islam

24

MACRA BANS RADIO ISLAM PROGRAM

20
Adil Chilungo

Are We Too Small for Political Courage?

July 24, 2025
The Great Muslim Defection: How Malawian Muslims Are Abandoning UDF Loyalty

๐—›๐—œ๐—ฆ๐—ง๐—ข๐—ฅ๐—œ๐—– ๐—ฉ๐—œ๐—–๐—ง๐—ข๐—ฅ๐—ฌ: ๐—–๐—ต๐—ฎ๐—ธ๐˜„๐—ฒ๐—ฟ๐—ฎ ๐——๐—ฒ๐—น๐—ถ๐˜ƒ๐—ฒ๐—ฟ๐˜€ ๐—ช๐—ต๐—ฎ๐˜ ๐Ÿฒ๐Ÿฌ ๐—ฌ๐—ฒ๐—ฎ๐—ฟ๐˜€ ๐—ผ๐—ณ ๐—Ÿ๐—ฒ๐—ฎ๐—ฑ๐—ฒ๐—ฟ๐˜€ ๐—ก๐—ฒ๐˜ƒ๐—ฒ๐—ฟ ๐—–๐—ผ๐˜‚๐—น๐—ฑโ€”๐—ข๐—ณ๐—ณ๐—ถ๐—ฐ๐—ถ๐—ฎ๐—น ๐—ฅ๐—ฒ๐—ฐ๐—ผ๐—ด๐—ป๐—ถ๐˜๐—ถ๐—ผ๐—ป ๐—ผ๐—ณ ๐—˜๐—ถ๐—ฑ ๐—ฎ๐—น-๐—”๐—ฑ๐—ต๐—ฎ

June 7, 2025
The Wrong Sacrifice: How Muslims in Malawi Are Slaughtering Community Unity Instead of Goats This Eid

The Wrong Sacrifice: How Muslims in Malawi Are Slaughtering Community Unity Instead of Goats This Eid

June 5, 2025
The Stage He Chose: Dr. Namadingo’s Unscripted Performance in Wakata

The Stage He Chose: Dr. Namadingo’s Unscripted Performance in Wakata

May 10, 2025

Connect

Recent News

Adil Chilungo

Are We Too Small for Political Courage?

July 24, 2025
The Great Muslim Defection: How Malawian Muslims Are Abandoning UDF Loyalty

๐—›๐—œ๐—ฆ๐—ง๐—ข๐—ฅ๐—œ๐—– ๐—ฉ๐—œ๐—–๐—ง๐—ข๐—ฅ๐—ฌ: ๐—–๐—ต๐—ฎ๐—ธ๐˜„๐—ฒ๐—ฟ๐—ฎ ๐——๐—ฒ๐—น๐—ถ๐˜ƒ๐—ฒ๐—ฟ๐˜€ ๐—ช๐—ต๐—ฎ๐˜ ๐Ÿฒ๐Ÿฌ ๐—ฌ๐—ฒ๐—ฎ๐—ฟ๐˜€ ๐—ผ๐—ณ ๐—Ÿ๐—ฒ๐—ฎ๐—ฑ๐—ฒ๐—ฟ๐˜€ ๐—ก๐—ฒ๐˜ƒ๐—ฒ๐—ฟ ๐—–๐—ผ๐˜‚๐—น๐—ฑโ€”๐—ข๐—ณ๐—ณ๐—ถ๐—ฐ๐—ถ๐—ฎ๐—น ๐—ฅ๐—ฒ๐—ฐ๐—ผ๐—ด๐—ป๐—ถ๐˜๐—ถ๐—ผ๐—ป ๐—ผ๐—ณ ๐—˜๐—ถ๐—ฑ ๐—ฎ๐—น-๐—”๐—ฑ๐—ต๐—ฎ

June 7, 2025
The Wrong Sacrifice: How Muslims in Malawi Are Slaughtering Community Unity Instead of Goats This Eid

The Wrong Sacrifice: How Muslims in Malawi Are Slaughtering Community Unity Instead of Goats This Eid

June 5, 2025

Faith Podcast

Swalah 101

Ramadhan

Akudziwanji Za Chisilamu

Islamic Finance

Categories

  • Analysis
  • Business
  • Column
  • Crime and Society
  • Culture
  • Economy
  • Education
  • Entertainment
  • Featured
  • General
  • Health
  • International
  • Lifestyle
  • Opinion
  • Politics
  • Religion
  • Sports
  • Travel

News in Pictures

Amir Jakhura
Amir Jakhura Addressing the Journalists
Some of the beneficiaries

ยฉ 2022 Malawi Muslims Official Website -Website by Freelance Web Solutions.

No Result
View All Result
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World

ยฉ 2022 Malawi Muslims Official Website -Website by Freelance Web Solutions.

Welcome Back!

Login to your account below

Forgotten Password?

Retrieve your password

Please enter your username or email address to reset your password.

Log In

Add New Playlist

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00

Queue

Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00