Malawi Muslims Official Website
No Result
View All Result
  • Login
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World
Contact Us
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World
No Result
View All Result
Malawi Muslims Official Website
No Result
View All Result
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World
Home Featured
Sheikh Idrissa Muhammad Apempha Asilamu Kuti Ayambe Kuthandiza Bungwe la MAM

Sheikh Idrissa Muhammad Apempha Asilamu Kuti Ayambe Kuthandiza Bungwe la MAM

Marshall Dyton by Marshall Dyton
1 year ago
in Featured, Religion
Reading Time: 2 mins read
A A
0
0
SHARES
252
VIEWS
Share on FacebookShare on TwitterShare on Whatsapp

Wapampando wa bungwe la Muslim Association of Malawi (MAM) Sheikh Idrissa Muhammad wapempha asilamu onse mdziko muno kuti ayambe kuthandiza bungweli.

RELATED POSTS

MAM Condoles Turkiye Over Earthquake Tragedy

Malawians Deserve Clean Water and Improved Sanitation – Abida Mia

Muslims Must Tap Into #Malawi2063 Opportunities

Sheikh Muhammad amalankhula izi pamsonkhano wa atolankhani womwe anachititsa lero mumzinda wa Blantyre.

Mtsogoleri wa asilamuyu wati ndizomvetsa chisoni kuti pali kagulu kena ka asilamu komwe kakumangonena zoyipa za MAM, kunena kuti akuluakulu abungweli akusakaza ndalama chikhalirenicho sanasonkheko ndalama iliyonse.

Iwo anati poyerekeza ndi mabungwe ena oti si asilamu, MAM imadalira thandizo lake kuchokera kwa mabungwe akunja kwa dziko lino ndipo ndalama zake zimakhala ndi ntchito zake kale.

“Asilamu tisinthe maganizidwe athu. Tisamangokamba zoipa za bungwe, kulikakamiza kuti lipange zinthu zoti silingakwanitse kumakhala kuti palibe chomwe timapereka ku bungweli. Kodi ndi ndani ananena kuti poti ndife asilamu ndiye tizingolandira za ulere koma kupereka ayi popeza kuti Chipembedzo chachisilamu ndiye chimalimbikitsa kuperekako? Tangoganizani nthawi ya Qurban munthu kumachoka kutali ngati ku Lilongwe, kuthira mafuta muchigalimoto chodhula kubwera ku Blantyre kukalandira Mbuzi imodzi? Ndalama mwagula mafuta sangakwanitse kugula Mbuzi olo imodzi zoona? Izi sizoona ayi,” atero mtsogoleriyu.

Sheikh Muhammad anawonjezerapo kunena kuti pamene amatenga mpandowu zaka khumi zapitazo analamula atsogoleri amadera onse mdziko muno kuti atsegule ma akaunti akubanki ndi cholinga choti asilamu ayambe kusonkha ndipo kuti ndalamayo izigwiritsidwa popangira zitukuko zing’onozing’ono za deralo.

“Kutha kumva chisoni kumva kuti chitsegulireni akauntiyi sikunaloweko olo ndalama iliyonse mpaka abanki anatseka ma akaunti. Koma lero akubwera ndikumandinyoza ine kuti ndikuba ndalama za asilamu mdziko muno. Ndalama zake ziti popeza simunaperekeko ndalama iliyonse?” Anafunsa motero Sheikh Muhammad.

Mtsogoleriyu anapitilizanso kunena kuti kwa amene ali ndi umboni okwanira woti iwo akusakaza ndalama za asilamu apite ndi umboni ku polisi yomwe ali nayo pafupi kukang’amala.

ADVERTISEMENT

“Akanene kuti Sheikh Idrissa Muhammad analandira ndalama izi za asilamu komwe ntchito yake sanagwiritse ndipo umboni wake ndi uwu mmalo momangolankhulalankhula mmasamba amchezo,” atero mtsogoleri wa asilamuyu.

Iye anati sakuletsa aliyense kupereka madandaulo ake ku bungweli, kunena kuti khomo ndi lotsegula.

“Atha kuyamba kuwapeza atsogoleri amadela akukhala omwe adzatenge nkhawazo kupititsa kulikulu. Sindinganene kuti ndine mNgelo wosalakwa. Ndili ndi zofooka zanga koma tiyeni titsatire njira yoyenera osati kundiopsyeza kuti mundipha. Mundipha chifukwa chani?” Anadandaula motero Sheikh Idrissa Muhammad.

ShareTweetSend

Related Posts

MAM Condoles Turkiye Over Earthquake Tragedy
Featured

MAM Condoles Turkiye Over Earthquake Tragedy

by Bright Malenga
February 7, 2023
0
0

The national chairman of the Muslim Association of Malawi (MAM) His Eminence Sheikh Idrissa Muhammad has condoled Turkiye following earthquake...

Read more

Malawians Deserve Clean Water and Improved Sanitation – Abida Mia

Muslims Must Tap Into #Malawi2063 Opportunities

Muslims Urged to Spread Islam

Mangochi Graduates Vow to Inspire Students

Chakwera Needs Ministers to Practice Servant Leadership

Next Post
Government Hails QMAM’s HIV/AIDS Project in Machinga

Government Hails QMAM's HIV/AIDS Project in Machinga

Sudan Graduates for Bigger Social Projects

Sudan Graduates for Bigger Social Projects

  • Organisation Drills Borehole in Balaka District: Urges Organisations to Develop Rural Areas

    Organisation Drills Borehole in Balaka District: Urges Organisations to Develop Rural Areas

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Seek Knowledge Regardless of Age – Muslims Advised

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Fuel Prices Go Up in Malawi

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Police warn Malawians against sending money to unknown Facebook friends

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • LMJ Medicals for State-of-the-art Hospital

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Trending
  • Comments
  • Latest
Organisation Drills Borehole in Balaka District: Urges Organisations to Develop Rural Areas

Organisation Drills Borehole in Balaka District: Urges Organisations to Develop Rural Areas

July 28, 2022
Seek Knowledge Regardless of Age – Muslims Advised

Seek Knowledge Regardless of Age – Muslims Advised

May 11, 2022
Fuel Prices Go Up in Malawi

Fuel Prices Go Up in Malawi

March 8, 2021
Police warn Malawians against sending money to unknown Facebook friends

Police warn Malawians against sending money to unknown Facebook friends

December 24, 2019

Malawian Muslims Chased at Asian Muslims Milad–un-Nabee Feast

78

Supreme Council of Ulama Says Eid Adha Tuesday

28

Fatima Rajab the Guardian Angel, Abandoned for Refusing to Denounce Islam

24

MACRA BANS RADIO ISLAM PROGRAM

20
MAM Condoles Turkiye Over Earthquake Tragedy

MAM Condoles Turkiye Over Earthquake Tragedy

February 7, 2023
Malawians Deserve Clean Water and Improved Sanitation – Abida Mia

Malawians Deserve Clean Water and Improved Sanitation – Abida Mia

February 7, 2023
Muslims Must Tap Into #Malawi2063 Opportunities

Muslims Must Tap Into #Malawi2063 Opportunities

February 6, 2023
Muslims Urged to Spread Islam

Muslims Urged to Spread Islam

February 5, 2023

Connect

Recent News

MAM Condoles Turkiye Over Earthquake Tragedy

MAM Condoles Turkiye Over Earthquake Tragedy

February 7, 2023
Malawians Deserve Clean Water and Improved Sanitation – Abida Mia

Malawians Deserve Clean Water and Improved Sanitation – Abida Mia

February 7, 2023
Muslims Must Tap Into #Malawi2063 Opportunities

Muslims Must Tap Into #Malawi2063 Opportunities

February 6, 2023

Faith Podcast

Islamic Finance

Swalah 101

Akudziwanji Za Chisilamu

Ramadhan

Categories

  • Analysis
  • Business
  • Column
  • Crime and Society
  • Culture
  • Economy
  • Education
  • Entertainment
  • Featured
  • General
  • Health
  • International
  • Opinion
  • Politics
  • Religion
  • Sports
  • Travel

News in Pictures

Amir Jakhura
Amir Jakhura Addressing the Journalists
Some of the beneficiaries

© 2022 Malawi Muslims Official Website -Website by Freelance Web Solutions.

No Result
View All Result
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World

© 2022 Malawi Muslims Official Website -Website by Freelance Web Solutions.

Welcome Back!

Login to your account below

Forgotten Password?

Retrieve your password

Please enter your username or email address to reset your password.

Log In

Add New Playlist

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00

Queue

Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00
Go to mobile version