Malawi Muslims Official Website
No Result
View All Result
  • Login
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World
Contact Us
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World
No Result
View All Result
Malawi Muslims Official Website
No Result
View All Result
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World
Home Featured
Sheikh Idrissa Muhammad Apempha Asilamu Kuti Ayambe Kuthandiza Bungwe la MAM

Sheikh Idrissa Muhammad Apempha Asilamu Kuti Ayambe Kuthandiza Bungwe la MAM

Marshall Dyton by Marshall Dyton
3 years ago
in Featured, Religion
Reading Time: 2 mins read
A A
0
0
SHARES
0
VIEWS
Share on FacebookShare on TwitterShare on Whatsapp

Wapampando wa bungwe la Muslim Association of Malawi (MAM) Sheikh Idrissa Muhammad wapempha asilamu onse mdziko muno kuti ayambe kuthandiza bungweli.

RELATED POSTS

Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

From 13 Points to Nation-Builder: Habibu’s Journey of Purpose

Sacred Care: Muslim Nurse’s Mission of Mercy

Sheikh Muhammad amalankhula izi pamsonkhano wa atolankhani womwe anachititsa lero mumzinda wa Blantyre.

Mtsogoleri wa asilamuyu wati ndizomvetsa chisoni kuti pali kagulu kena ka asilamu komwe kakumangonena zoyipa za MAM, kunena kuti akuluakulu abungweli akusakaza ndalama chikhalirenicho sanasonkheko ndalama iliyonse.

Iwo anati poyerekeza ndi mabungwe ena oti si asilamu, MAM imadalira thandizo lake kuchokera kwa mabungwe akunja kwa dziko lino ndipo ndalama zake zimakhala ndi ntchito zake kale.

“Asilamu tisinthe maganizidwe athu. Tisamangokamba zoipa za bungwe, kulikakamiza kuti lipange zinthu zoti silingakwanitse kumakhala kuti palibe chomwe timapereka ku bungweli. Kodi ndi ndani ananena kuti poti ndife asilamu ndiye tizingolandira za ulere koma kupereka ayi popeza kuti Chipembedzo chachisilamu ndiye chimalimbikitsa kuperekako? Tangoganizani nthawi ya Qurban munthu kumachoka kutali ngati ku Lilongwe, kuthira mafuta muchigalimoto chodhula kubwera ku Blantyre kukalandira Mbuzi imodzi? Ndalama mwagula mafuta sangakwanitse kugula Mbuzi olo imodzi zoona? Izi sizoona ayi,” atero mtsogoleriyu.

Sheikh Muhammad anawonjezerapo kunena kuti pamene amatenga mpandowu zaka khumi zapitazo analamula atsogoleri amadera onse mdziko muno kuti atsegule ma akaunti akubanki ndi cholinga choti asilamu ayambe kusonkha ndipo kuti ndalamayo izigwiritsidwa popangira zitukuko zing’onozing’ono za deralo.

“Kutha kumva chisoni kumva kuti chitsegulireni akauntiyi sikunaloweko olo ndalama iliyonse mpaka abanki anatseka ma akaunti. Koma lero akubwera ndikumandinyoza ine kuti ndikuba ndalama za asilamu mdziko muno. Ndalama zake ziti popeza simunaperekeko ndalama iliyonse?” Anafunsa motero Sheikh Muhammad.

Mtsogoleriyu anapitilizanso kunena kuti kwa amene ali ndi umboni okwanira woti iwo akusakaza ndalama za asilamu apite ndi umboni ku polisi yomwe ali nayo pafupi kukang’amala.

“Akanene kuti Sheikh Idrissa Muhammad analandira ndalama izi za asilamu komwe ntchito yake sanagwiritse ndipo umboni wake ndi uwu mmalo momangolankhulalankhula mmasamba amchezo,” atero mtsogoleri wa asilamuyu.

ADVERTISEMENT

Iye anati sakuletsa aliyense kupereka madandaulo ake ku bungweli, kunena kuti khomo ndi lotsegula.

“Atha kuyamba kuwapeza atsogoleri amadela akukhala omwe adzatenge nkhawazo kupititsa kulikulu. Sindinganene kuti ndine mNgelo wosalakwa. Ndili ndi zofooka zanga koma tiyeni titsatire njira yoyenera osati kundiopsyeza kuti mundipha. Mundipha chifukwa chani?” Anadandaula motero Sheikh Idrissa Muhammad.

ShareTweetSend

Related Posts

Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream
Analysis

Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

by Marshall Dyton
May 4, 2025
0
0

A peach-colored fence stands like a monument to broken promises in Mangochi. Green metal bars stretch between concrete pillars, framing...

Read more

From 13 Points to Nation-Builder: Habibu’s Journey of Purpose

Sacred Care: Muslim Nurse’s Mission of Mercy

The Great Muslim Defection: How Malawian Muslims Are Abandoning UDF Loyalty

Faith Under Siege: How Muslims Unknowingly Converted to Western Values

Silent Sacrifices: The Untold Story Of Malawi’s Sheikhs

  • edit post
    Sheikh Yahya

    Ya Sheikh, Can You Hear Us Weeping? A Community’s Heartfelt Farewell to Sheikh Hubdein Yahya

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Police warn Malawians against sending money to unknown Facebook friends

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Pastor Builds Grass-thatched Mosque

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • LMJ Medicals for State-of-the-art Hospital

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Lack of Mosque Worries Former Pastor

    0 shares
    Share 0 Tweet 0
  • Trending
  • Comments
  • Latest
edit post
Sheikh Yahya

Ya Sheikh, Can You Hear Us Weeping? A Community’s Heartfelt Farewell to Sheikh Hubdein Yahya

April 4, 2025
edit post
Police warn Malawians against sending money to unknown Facebook friends

Police warn Malawians against sending money to unknown Facebook friends

December 24, 2019
edit post
Pastor Builds Grass-thatched Mosque

Pastor Builds Grass-thatched Mosque

January 15, 2024
edit post

LMJ Medicals for State-of-the-art Hospital

December 6, 2015
edit post

Malawian Muslims Chased at Asian Muslims Milad–un-Nabee Feast

78
edit post

Supreme Council of Ulama Says Eid Adha Tuesday

28
edit post

Fatima Rajab the Guardian Angel, Abandoned for Refusing to Denounce Islam

24
edit post

MACRA BANS RADIO ISLAM PROGRAM

20
edit post

IERA Malawi Drills UNIMA Students in Daawah

May 5, 2025
edit post
Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

May 4, 2025
edit post
From 13 Points to Nation-Builder: Habibu’s Journey of Purpose

From 13 Points to Nation-Builder: Habibu’s Journey of Purpose

May 2, 2025
edit post
From Chayamba to UNIMA: Hawa Yusuf’s Journey of Resilience and Purpose

From Chayamba to UNIMA: Hawa Yusuf’s Journey of Resilience and Purpose

May 2, 2025

Connect

Recent News

edit post

IERA Malawi Drills UNIMA Students in Daawah

May 5, 2025
edit post
Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

Broken Trust: How Lack Of Transparency Derailed The Mufti-Abbas University Dream

May 4, 2025
edit post
From 13 Points to Nation-Builder: Habibu’s Journey of Purpose

From 13 Points to Nation-Builder: Habibu’s Journey of Purpose

May 2, 2025

Faith Podcast

edit podcast

Islamic Finance

edit podcast

Swalah 101

edit podcast

Akudziwanji Za Chisilamu

edit podcast

Ramadhan

Categories

  • Analysis
  • Business
  • Column
  • Crime and Society
  • Culture
  • Economy
  • Education
  • Entertainment
  • Featured
  • General
  • Health
  • International
  • Lifestyle
  • Opinion
  • Politics
  • Religion
  • Sports
  • Travel

News in Pictures

Amir Jakhura
Amir Jakhura Addressing the Journalists
Some of the beneficiaries

© 2022 Malawi Muslims Official Website -Website by Freelance Web Solutions.

No Result
View All Result
  • Home
  • Religion
  • Business
  • Health
  • Education
  • Entertainment
  • Politics
  • Sports
  • World

© 2022 Malawi Muslims Official Website -Website by Freelance Web Solutions.

Welcome Back!

Login to your account below

Forgotten Password?

Retrieve your password

Please enter your username or email address to reset your password.

Log In

Add New Playlist

Are you sure want to unlock this post?
Unlock left : 0
Are you sure want to cancel subscription?
-
00:00
00:00

Queue

Update Required Flash plugin
-
00:00
00:00